Awa ndi mayeso oyesedwa. Apambaneni kuti mupeze mfundo zopita ku Satifiketi ya Chivomerezo cha Utumiki yanu.
Ahebri 11:6 — Ndipo popanda chikhulupiriro nʼkosatheka kukondweretsa Mulungu, chifukwa aliyense amene amabwera kwa Iye ayenera kukhulupirira kuti Mulungu alipodi ndi kuti Iye amapereka ________ kwa amene akumufunitsitsa.
wosatha
utumiki
mphotho
Miyambo 11:27 — Iye amene amafunafuna zabwino mwakhama ________ zabwinozo, koma wofunafuna zoyipa zidzamupeza.
Amasunga
amapeza
amadana
Masalimo 63:1 — Inu Mulungu, ndinu Mulungu wanga, moona mtima ine ndimakufunafunani; moyo wanga uli ndi ludzu lofuna Inu, ________ langa likulakalaka inu, mʼdziko lowuma ndi lotopetsa kumene kulibe madzi.
thupi
yekha
ulemu
Masalimo 78:34 — Mulungu atawapha, iwo amamufunafuna Iyeyo; iwo ankatembenukiranso kwa Iye ________.
mwachangu
anatsogolera
kuwerengedwa
Miyambo 8:19 — Chipatso changa ndi chabwino kuposa golide, ngakhale golide wosalala; zimene ine ndimabereka zimaposa ________ wabwino kwambiri.
chisoni
siliva
mphatso
Deuteronomo 6:17 — Onetsetsani kuti mukusunga ________ a Yehova Mulungu wanu, malangizo ake ndi zikhazikitso zake zimene anakulamulirani.
mitundu
adani
malamulo
Deuteronomo 11:13 — Choncho mukasunga ________ malamulo amene ndikukupatsani lero lino, kukonda Yehova Mulungu wanu ndi kumutumikira Iyeyo ndi mtima wanu wonse ndi moyo wanu wonse
mwachilungamo
zokoma
mokhulupirika
Yoswa 22:5 — Koma samalitsani kuti mumvere malamulo ndi malangizo amene Mose mtumiki wa Yehova anakupatsani: kukonda Yehova Mulungu wanu, kuchita zimene iye amafuna, ________ malamulo ake, kukhala okhulupirika kwa Iye ndi kumutumikira ndi mtima wanu wonse ndi moyo wanu wonse.”
Machitidwe a Atumwi 17:11 — Tsopano anthu a ku Bereya anali akhalidwe labwino kusiyana ndi Atesalonika, pakuti iwo analandira mawu ndi chidwi chachikulu ndipo ankasanthula ________ tsiku ndi tsiku kuti aone ngati zimene ankanena Paulozo zinali zoona.
mtsikana
Malemba
anakumana
Luka 15:8 — “Kapena tiyeni tifanizire mayi amene anali ndi ndalama zasiliva khumi ndipo imodzi nʼkutayika, kodi sayatsa ________ ndi kusesa mʼnyumba ndi kufuna mosamalitsa mpaka atayipeza?
mbiri
Atate
nyale
Machitidwe a Atumwi 20:24 — Koma sindilabadira konse za moyo wanga ngati kuti ndi wa mtengo wapatali kwa ine, malingana ndikatsirize ntchito yanga ndi ________ umene Ambuye Yesu anandipatsa, ntchito yochitira umboni Uthenga Wabwino wachisomo cha Mulungu.
utumiki
kuchiritsa
dera
2 Timoteyo 4:5 — Koma iwe, khala tcheru nthawi zonse, pirira mʼzovuta, gwira ntchito ya ________, gwira ntchito zonse za utumiki wako.
Chivumbulutso 2:10 — Musachite mantha ndi zimene muti musauke nazo posachedwapa. Ndithu, ________ adzayika ena a inu mʼndende pofuna kukuyesani, ndipo mudzazunzika kwa masiku khumi. Khalani okhulupirika ngakhale zitafika pa imfa, ndipo Ine ndidzakupatsani chipewa cha ulemerero wamoyo.
Ziyoni
Pilato
Satana
2 Timoteyo 4:18 — Ambuye adzandilanditsa ku chilichonse chofuna kundichita choyipa ndipo adzandisamalira bwino mpaka kundilowetsa chonse mu ufumu wake ________. Kwa Iye kukhale ulemerero mpaka muyaya.