Awa ndi mayeso oyesedwa. Apambaneni kuti mupeze mfundo zopita ku Satifiketi ya Chivomerezo cha Utumiki yanu.
Yesaya 9:6 — Chifukwa mwana watibadwira, mwana wamwamuna wapatsidwa kwa ife, ndipo ulamuliro udzakhala pa phewa lake. Ndipo adzamutcha dzina lake lakuti Phungu ________, Mulungu Wamphamvu, Atate Amuyaya, ndi Mfumu ya Mtendere.
okongola
onyansa
Wodabwitsa
Genesis 1:26 — Zitatha izi Mulungu anati, “Tipange munthu mʼchifanizo chathu, mofanana ndi ife kuti alamulire nsomba za ________, mbalame zamlengalenga, nyama zonse zoweta ndi zonse zokwawa za pa dziko lapansi ndi zamoyo zonse zakutchire.”
uvuni
mʼnyanja
ngʼombe
Yohane 1:18 — Palibe munthu amene anaona Mulungu, koma Mwana mmodzi yekhayo amene ali wa pamtima pa ________, ndiye anafotokoza za Iye.
Atate
makolo
mlandu
Malaki 3:1 — Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Ine ndidzatuma mthenga wanga amene adzakonza ________ pamaso panga. Kenaka mwadzidzidzi Ambuye amene mukumufunafuna adzafika ku Nyumba yake. Mthenga wapangano amene mukumuyembekezera adzabwera.”
abambo
njira
mbuye
Genesis 22:2 — Ndipo Mulungu anati, “Tenga ________, mwana wako yekhayo amene umamukonda ndi kupita naye ku dziko la Moriya. Ukamupereke iye ngati nsembe yopsereza pa limodzi la mapiri a kumeneko limene ndidzakuwuza.”
Yohane 1:29 — Pa tsiku lotsatira Yohane anaona Yesu akubwera kwa iye ndipo anati, “Taonani, Mwana ________ wa Mulungu, amene achotsa tchimo la dziko lapansi!
Wankhosa
zipatso
yekha
Yesaya 53:7 — Anthu anamuzunza ndi kumusautsa, koma sanayankhule kanthu. Monga mwana ________ wopita naye kokamupha amachitira, kapena monga nkhosa imakhalira duu poyimeta, momwemonso iye sanatsekule pakamwa pake.
Mika 5:2 — “Koma iwe ________ Efurata, ngakhale uli wonyozeka pakati pa mafuko a Yuda, mwa iwe mudzatuluka munthu amene adzalamulira Israeli, amene chiyambi chake nʼchakalekale, nʼchamasiku amakedzana.”
Yufurate
Betelehemu
Giligala
Genesis 3:15 — Ndipo ndidzayika chidani pakati pa iwe ndi mkaziyo, pakati pa mbewu yako ndi mbewu yake; Iye adzaphwanya ________ wako ndipo iwe udzaluma chidendene chake.”
mapazi
pakamwa
mutu
Yohane 1:14 — Mawu anasandulika ________ ndipo anakhala pakati pathu. Ife tinaona ulemerero wake, ulemerero wa Iye amene ndi Mwana mmodzi yekhayo wa Atate, wodzaza ndi chisomo ndi choonadi.
mapazi
mnzake
thupi
Akolose 2:9 — Pakuti mʼthupi la Khristu ________ umulungu wonse wathunthu.
1 Timoteyo 2:5 — Pakuti pali Mulungu mmodzi yekha ndi ________ mmodzi yekha pakati pa Mulungu ndi anthu, munthu uja Khristu Yesu.
achigololo
odziletsa
Mʼkhalapakati
Ahebri 1:8 — Koma za Mwana wake akuti, “Inu Mulungu, mpando wanu ________ udzakhala mpaka muyaya, ndipo mudzaweruza molungama mu ufumu wanu.
adani
dzanja
waufumu
Masalimo 110:1 — Yehova akuwuza Mbuye wanga kuti, “Khala ku dzanja langa lamanja mpaka nditasandutsa adani ako kukhala ________ mapazi ako.”
chopondapo
mdzakazi
magulu
1 Akorinto 15:20 — Koma nʼzoonadi kuti Khristu anaukitsidwa kwa kufa, chipatso choyamba cha onse ogona ________.
mipingo
tulo
moni
Akolose 1:27 — Kwa iwo amene Mulungu anawasankha kuti awadziwitse pakati pa a mitundu ina, ulemerero wa chuma cha chinsinsi ichi, amene ndi Khristu mwa inu, ________ cha ulemerero.
chiyembekezo
chisomo
thupi
Chivumbulutso 1:7 — “Onani akubwera ndi ________,” ndipo “Aliyense adzamuona, ndi amene anamubaya omwe.” Ndipo anthu a mitundu yonse ya pa dziko lapansi “adzalira chingʼangʼadza chifukwa cha Iye.” Zidzakhaladi momwemo, Ameni.
tsitsi
malemba
mitambo
Yohane 3:16 — “Pakuti Mulungu anakonda dziko lapansi, kotero anapereka Mwana wake wobadwa yekha, kuti aliyense wokhulupirira Iye asatayike koma akhale ndi moyo ________.