2 Petro 1:5-6 — Choncho, chitani khama kuwonjezera moyo wabwino pa ________ chanu, ndipo pa moyo wabwino muwonjezerepo nzeru.
chiyembekezo
chikhulupiriro
ulemu
Luka 8:15 — Koma mbewu za pa nthaka yabwino zikuyimira anthu amene ali ndi mtima woona ndi wabwino, amene amamva mawu nawasunga, ndipo amalimbikira mpaka amabala ________.
zipatso
chikondi
mtendere
Yesaya 30:18 — Komatu Yehova akufunitsitsa kuti akukomereni mtima, iye ali wokonzeka kuti akuchitireni ________. Pakuti Yehova ndi Mulungu wachilungamo. Ndi odala onse amene amakhulupirira Iye!
ulemerero
dzanja
chifundo
Masalimo 40:1 — ________ ndinadikira Yehova Iye anatembenukira kwa ine ndipo anamva kulira kwanga.
Mofatsa
mwamphamvu
zokoma
Maliro 3:25 — Yehova ndi wabwino kwa amene amayembekezera Iye, kwa munthu amene ________ Iyeyo;
Amasunga
amafunafuna
amadana
Maliro 3:26 — nʼkwabwino kudikira ________ cha Yehova modekha.
Akolose 3:12 — Choncho, ngati anthu osankhidwa ndi Mulungu, oyera mtima ndi okondedwa kwambiri, muvale chifundo, kukoma mtima, kudzichepetsa, ________ ndi kupirira.
mʼmayesero
kufatsa
vumbulutso
Aefeso 4:2 — Mukhale odzichepetsa kwathunthu ndi ofatsa; mukhale oleza mtima, ololerana wina ndi ________ mwachikondi.
Atate
mlandu
mnzake
Akolose 1:11 — Timapempheranso kuti Mulungu akulimbikitseni ndi mphamvu yake yonse ya ________ wake, kuti muzipirira zonse ndi mitima yofatsa ndi ya chimwemwe
ulemerero
mtendere
mantha
Agalatiya 5:22 — Koma chipatso cha Mzimu Woyera ndi chikondi, chimwemwe, mtendere, kuleza mtima, chifundo, kukoma mtima, ________
Mlaliki 7:8 — Mathero ake a chinthu ndi abwino kupambana chiyambi chake, ndipo ________ nʼkwabwino kupambana kudzikuza.
chimwemwe
kufatsa
chete
Yakobo 5:7 — Tsono abale, pirirani mpaka kubwera kwa Ambuye. Onani mmene amachitira mlimi. Amadikirira kuti ________ zabwino zioneke mʼmunda mwake. Amayembekezera mokhazikika mtima kuyambira nthawi ya mvula yoyamba mpaka yotsiriza.
mtendere
chisomo
zipatso
Ahebri 12:1 — Tsono popeza ifenso tazunguliridwa ndi gulu lalikulu la mboni, tiyeni titaye chilichonse chimene chimatitchinga, ________ tchimo limene limatikola mosavuta, ndipo tithamange ndi khama mpikisano umene tayambawu.
makamaka
okondedwa
mwamphamvu
Ahebri 12:2 — Tiyeni tiyangʼanitsitse Yesu, amene ndi woyamba ndi wotsiriza wa chikhulupiriro chathu. Chifukwa cha ________ chimene chimamudikira anapirira zowawa zapamtanda. Iye ananyoza manyazi a imfa yotere ndipo tsopano akukhala ku dzanja lamanja la mpando waufumu wa Mulungu.
chimwemwe
chipulumutso
mphamvu
Ahebri 12:3 — Muzilingalira za Iye amene anapirira udani waukulu chotere wochokera kwa anthu ________, kuti musafowoke ndi kutaya mtima.
mizimu
nyenyezi
ochimwa
Ahebri 10:36 — Nʼkofunika kuti mupirire kuti pamene muchita chifuniro cha Mulungu mudzalandire zimene Iye ________.
2 Timoteyo 2:4 — Palibe msilikali amene ali pa ntchito amagwiranso ntchito za anthu wamba, iye amafuna ________ bwana wolamulira.
kupitiriza
kukondweretsa
kulemekeza
2 Timoteyo 2:10 — Choncho ndikupirira chilichonse chifukwa cha osankhidwa, kuti nawonso apulumutsidwe ndi Khristu Yesu ndi kulandira ulemerero ________.
ukapolo
wosatha
chigololo
Chivumbulutso 14:12 — Pamenepa ndi pofunika kupirira kwa anthu oyera mtima amene amasunga ________ a Mulungu ndi kukhalabe okhulupirika kwa Yesu.
njira
malamulo
nkhosa
Yesaya 40:31 — koma iwo amene ________ Yehova adzalandira mphamvu zatsopano. Adzawuluka ngati chiwombankhanga; adzathamanga koma sadzalefuka, adzayenda koma sadzatopa konse.