Awa ndi mayeso oyesedwa. Apambaneni kuti mupeze mfundo zopita ku Satifiketi ya Chivomerezo cha Utumiki yanu.
MATEYU 16:17 — Yesu anati kwa iye, “Ndiwe wodala Simoni mwana wa ________, popeza si munthu amene anakuwululira izi koma Atate anga akumwamba.
Zebedayo
Aramu
Yona
YOHANE 6:44 — Palibe munthu amene angabwere kwa Ine, ngati ________ amene anandituma Ine samubweretsa. Ndipo Ine ndidzamuukitsa kwa akufa pa tsiku lomaliza.
Khristu
makolo
Atate
AROMA 10:17 — Motero, ________ chimabwera pamene timva uthenga ndipo uthenga umamveka kuchokera ku mawu a Khristu.
mtendere
thupi
chikhulupiriro
1 PETRO 2:2 — Monga ________ obadwa kumene amalirira mkaka, inunso muzilakalaka mkaka weniweni wauzimu, kuti mukule ndi kukufikitsani ku chipulumutso chanu
mipando
makanda
zikho
YOHANE 17:3 — Tsono moyo ________ ndi uwu: Iwo akudziweni Inu, Mulungu yekhayo woona, ndi Yesu Khristu, amene Inu mwamutuma.
lionse
wosathawo
achifwamba
MACHITIDWE A ATUMWI 4:13 — Ataona kulimba mtima kwa Petro ndi ________ ndi kuzindikira kuti anali osaphunzira, anthu wamba, anadabwa kwambiri ndipo anazindikira kuti anthuwa anakhala pamodzi ndi Yesu.
Yakobo
Hananiya
Yohane
MATEYU 11:28 — “Idzani kwa Ine, inu nonse otopa ndi ________ ndipo Ine ndidzakupatsani mpumulo.
YOHANE 14:21 — Iye amene amadziwa malamulo anga ndi kuwasunga ndiye amene amandikonda. Wokonda Ine adzakondedwa ndi ________ wanga ndipo Inenso ndidzamukonda ndikudzionetsa ndekha kwa iye.”
Khristu
Atate
makolo
AKOLOSE 3:16 — Mawu a Khristu akhazikike kwathunthu mʼmitima mwanu. Muziphunzitsana ndi kulangizana wina ndi ________ ndi nzeru zonse pamene mukuyimba Masalimo, nyimbo zotamanda ndi nyimbo zauzimu, kuyimbira Mulungu ndi mitima yoyamika.
mlandu
mtanda
mnzake
MATEYU 10:32 — “Aliyense amene avomereza Ine pamaso pa anthu, Inenso ndidzavomereza pamaso pa ________ anga akumwamba.
Atate
Khristu
wantchito
MACHITIDWE A ATUMWI 5:41 — Iwo anachoka ku ________ Lalikulu akukondwa chifukwa anayesedwa oyenera kunyozedwa chifukwa cha dzina la Yesu.
mbalame
Bwalo
mʼnyanja
AROMA 12:1 — Nʼchifukwa chake ine ndikukupemphani abale, mwa chifundo cha Mulungu, kuti mupereke matupi anu monga ________ yamoyo, yopatulika ndi yokondweretsa Mulungu. Nsembeyi ndiye kupembedza kwanu kwa uzimu.
malo
nsembe
magazi
AROMA 8:35 — Ndani amene adzatilekanitsa ife ndi chikondi cha Khristu? Kodi ndi masautso, kapena zowawa, kapena mazunzo, kapena ________, kapena umaliseche, kapena choopsa, kapena lupanga?
njala
zovala
mbewu
CHIVUMBULUTSO 1:8 — “Ine ndine ________ ndi Omega,” akutero Ambuye Mulungu Wamphamvuzonseyo “amene muli, amene munalipo, ndi amene mudzakhalapo.”
Tiyatira
Laodikaya
Alefa
1 YOHANE 3:2 — Abale ________, tsopano ndife ana a Mulungu, ndipo sichinaoneke chimene tidzakhala. Koma tikudziwa kuti Yesu akadzaonekera, tidzafanana naye, pakuti tidzamuona Iyeyo monga momwe alili.
okondedwa
lapansi
mwamphamvu
YOBU 19:25 — Koma ndikudziwa kuti ________ wanga ali ndi moyo, ndipo pa nthawi yomaliza adzabwera kudzanditeteza.
mpulumutsi
mnzake
ukulu
YOHANE 8:12 — Yesu atayankhulanso kwa anthu, anati, “Ine ndine kuwunika kwa dziko ________. Aliyense amene anditsata Ine sadzayenda mu mdima, koma adzakhala ndi kuwala kotsogolera anthu ku moyo.”